5 prisoners bolt in Mulanje

Advertisement
prisoners

crime (2)Five prisoners have escaped in Mulanje district after they were left at the hospital to receive medication, Malawi police say.

Mulanje police spokesperson, James Kadadzera, refused to name the prisoners but he said there were six inmates at the hospital and one inmate refused the idea of escaping.

Kadadzera said the prisoner who stayed behind has two weeks remaining on his jail sentence and that could be the reason he did not escape.

The six prisoners were to stay at the hospital for two weeks to receive TB treatment.

 

Advertisement

45 Comments

  1. kkkkkkk Koma Zina ukamvaaaaaaaaaaa ! Iaiaiaiaiaiaiaiaaia

  2. If they were left alone without a prison warder, wat else can they do? Run away soldier basi. Komadi pachithunzipa akupitilira 5

  3. Kuthawa athawa koma chomwe chimavuta ndichinthu chimodzi usawone wa boma akungoziyendera uwona monga afuna iwe, so chenjerani muka saver x2 akakugwirani.

  4. kkkk munkhanimu mwati athawa 5 koma pa chithunzipa ndie gulu,ndie kuti amawapelekedza 5wo? Inutu mumanama mwamva ngati mulibe chithunzi cha nkhani yanu kulibwino kungolemba nkhani osaika chithuzi

  5. Malume nthumba la achimangalo munalakwitsa polingulitsa kwa nokha pamenepo munaba. Ndiyewo pokukalipirani amakukalipirani zoona

  6. Enao anawamanga zoti sanalakwe nde achita bho. If there was an ounce of justice left in this world then JB would be in prison by now

  7. muli boh koma mudzingopita ku moshiko mukapume kufikila pamene angazansiye udindo …
    ..ambuyangawa …….mulimbikile kutawako muwoloke chifukwa mw ndiochepatu atakhukugwila kawili

  8. Koma ndiyekuti kumeneko kunali kuthamangatu amwene, nanga sii by yoti live buleti ingandipeze ndisanakhote paja! Ayi choncho mwathawa ndithu bola asakupezeni, koma mkangochita zibwana akugwireni eeeeish mngawone mbwaza bwanji!

  9. Thanx alot prison escapers 4 the job wel done,u hv succesfully escaped..now u r about to participate round #2 which is #ManHunt

    1. Mlandu wake ungakhale wanji? Gross negligence kapena breach of peace or wa idle uja? paja a khoba akakwiya amangogawatu milandu.kkkk

  10. Akati mwayi sindiye kuti waponda wire nkukubaya,,,koma kuti waponda ndalama nkutola…Mwayiwawo athawawo,akukanika kumalizitsa kumanga a cash-gate ndiye kulibwanji oba mbuzi.

  11. zachamba basi!!!!!!!…

    anapusa bwanji apolisiwo? iwo anali kuti nthawo yomwe amathawa akaidi?
    aaaaaaaaaaaa

    zausilu

Comments are closed.