Public sex lands two in hands of police

Advertisement
sex

sexMalawi Police in the commercial city of Blantyre have arrested a man and a woman for having sex in a vehicle at a public place.

The two, Timothy Bonzo 29 and Liz Banda 23, were caught at it in a Toyota sprinter registration number BP 4009.

Confirming the development to Malawi24, Blantyre Police spokesperson Elizabeth Divala said the incident happened in the early hours of Sunday.

“The two were having sexual intercourse in a vehicle at Zodetsa bottle store around 03:30 hours,” said Divala.

The two are yet to appear before Blantyre magistrate court to answer charges of idle and disorderly contrary to section 180 of the penal code.

Bonzo hails from Mfera village, Tradition Authority (TA) Katunga, Chikwawa district while Banda comes from Chafilama village, TA Juma in Mulanje district.

 

Advertisement

145 Comments

  1. Vacab yongopangira mu mabar m’ma location mayazi. A police angofuna kuipitsa mbiri ya Timo coz anakana kuapatsa ndalama.
    Paja mumakonda kuauza anthu kuti azipulumutse okha mix maluzi kumachita kusowa yogulila chibuku fountain kapena kugula uniform yamwana ku school. Ntchito zinazi abale! Kkkkkkkk!

  2. haha iiiiiii koma kumalawi mwasowa chochita ndithu malo momateteza athu mziko muli bizy kugwila athu axigololo haha apolice akumalawi mukudya dollar zama halakkk

  3. Is This Picture Taken From Inside A Car?It Was Not Yet Morning And Obviously The Police Wanted To Steal Inside That Car And Fortunately They Found Job Inside!!!Wow

  4. It z unlawful to have sex in a public place, even if u r a married couple, BIG UP OUR MEN IN UNIFORM

  5. Tsono munthu atakhala kuti Ali ndi akazake, pa galimoto, nde atopa akufuna kugona koma alibe Ndalama yolipilira Ku nyumba ya alendo. Nde angoganiza zogona mgalimotomo, nde asapange mwambo wa ubatizo mugalimotomo?

  6. Never knew that’s an offense, go around pubs that’s what we are doing all night long

  7. Mulilongwemuno inu apolice mwakhala mukupanga ma roadbrk adzidzidzi usiku koma palibe chimene munauzapo ntundu wamalawi kuti mwagwila,koma pafupifupi dairy usiku mukunka mutseka miseu nkumati mukupanga chipikisheni……shupt zanu…kuba basi,inu mugalimotomo munawaona bwanji?

  8. Anthu opusa ndio amavera ndkukhulupilila amalawi 24.anthu angamakwerane chotani kunsi kwakafamily car ngat kmeneka,sndlo bodzalo limenelo?musawade apolice coz of ur false stories.apolice akwathu kuno amagwila ntchito yao mwachilungamo. Zachamba zanuzo osadzaikaso mwanva?

  9. Nanga bwanji sitimamva kuti apolisi agwira anthu patchire kapena mu office? Nchifukwa chiani police yathu imalimbana kwambiri ndi magalimoto? Kodi tinene kuti milandu yeniyeni ikusowa?

  10. Apolice u are disgrace umbanda onseu ukukanikani mukalimbane ndi akuluakulu ogwirizana mugalimoto yawo usiku eeeshi u dissapoint me

  11. simuchita manyazi mukamanena zaboza nanga umu ndi m,galimoto? ngati mwatha maplan muzikalima kumudzi minda ya azgogo anu aja ikukudikilani

  12. Ana apachire samaona cholakwika kapena samaziwa tanthauzo LA public place a police agwira nchito yotamandika akhoti ndi amene akagamule.

  13. enanu muziyendako muziona zomwe zikuchitika mmaiko anzathu.osamangothamangira kutukwana ndi ma fundoles apa. maiko enawa olo kuyenda ndi botolo la mowa mmanja osaika mu bag kapena mjumbo kukumanga.public drinking.what more sex in the calb.mukamatukwana zinazi nkumaxiona inu ozindikira. akuyenera ayankhe milandu basi.sanalemekeze umunthu. better akanaimika pa ka tchire galimoyo.ikanakhala njira ina.

  14. Dziko la malawi silotsalila pauzimu ngati maiko enawo akupanga zigololo public ndiyekut akutsalila muuzimu,malawi police gwilani ntchito yanu ok ok

  15. M,maiko anzathu apolice sakhala busy ndizimenezi,iwo amalimbana ndi akuba komanso zigawenga koma kuno kwathu ku NYASALANDE apolice akatero amati agwira ntchito,mwinanso anthuwo anakana kupereka zam’manja paja apolice ali ndimkhalidwe omuuza munthu kuti “dzipulumutse wekha”

  16. What’s Wrong After All It Was At Night… Ma Galimoto Akumatha Mashokowa Mmesa Enawa Akuthera Zomwezo! Leave Them Alone Coz By Going Into Th Car At Night, They Were Excluded From The Public. Bwerani Ku Chez Muzamanga Anthu Mpaka Kutopa

  17. A car is a private property. I also did it on Saturday but nobody can arrest me. Maybe it was a bakkie so the encounter was in the body but sedan is free for bonking

  18. Prophet Shepherd Bushiri I was praying few minutes ago and I saw the soil shaking and it seemed like an earthquake. I saw many houses falling down and many lives lost. My prayer partners all over the world let’s pray for Africa. you and me can stop anything that is bad from happening. As days approaches I will tell you more in details so that we can resist it in prayer in Jesus name. Shalom

    1. Zopusa Mwai.Bushiri anthu ovulala mu church mwake anawatumiza kuchipatala bwanji,mmalo moti awachize iyeyo awapemphelere.Kupepera

  19. The charge is”idle and disorderly”.Free these people because they were not “idle”when having sexual intercourse neither “disorderly”because they doing it in the privacy of their own car.Find another charge
    which will hold water. There’re sharp defence Layers these days.

Comments are closed.