Annie Matumbi dresses Maskal down

Advertisement
Annie Matumbi
Annie Matumbi
Matumbi: Talks ill about Maskal.

Malawian artist and Times Television presenter Annie Matumbi who is popularly known for mocking fellow artists, has been at again as he has openly ashamed afro-pop icon Maskal.

During a live broadcast of “Urban trend” programme yesterday, Matumbi whose real name is Chiyanjano Muhezuwa, uttered words which may be hardly accommodated in Maskal’s ears.

His ill language followed from the “Udalire” video by Maskal, when it came to an end, Matumbi could not help but go off-track to mock the Udalire star concerning his live perfomance.

“Ameneyo ndi Maskal akuti udalire. Nthawi imeneyi anatchuka Maskal aliyese kumangoti Maska! Maskal! koma pa stage kulepheleratu, samatha ata, (that is Maskal. He was man of the people when he released this video but when it came to live performance, he was as good as nothing), ” said Matumbi

Matumbi is considered to be an artist who uses sarcasm against fellow artists.

However the audience is meant to understand that he does not mean it.

A few years ago, he released a song which exposed mistakes by other artists on the claim that they are all his friends hence the liberty to make fun of them.

Advertisement

166 Comments

  1. Ummmh Man 2mbi! Reality talking z wat we bliv in. Ndimakufila man. Ngati ukunama ntchentche indizomphe pa msanapa!

  2. guys 2mbi sakunama and u knw it,kma an2 omwe mumamkonda maskal smukufuna kuvomereza ngamo,,,! maskal amatha kuimba kma pa stage zmamukanika,tinenepo ngamo apa..! amene mukumunena 2mbi kt walakwitsa mongozitaisa nthaw,coz iwowo nzot amachezerana,inu mul bzy ku bwebwetuka apa…! osangozisia bwanji,ainakewo akuziwana..!

  3. #Maskal is the biggest part of my playlist. I wl never stop buying n listening t his musik, even goin t his shows……. #Maskalslingjay

  4. I thought being a broad caster is about being a man for the people, not a selfie… He aught to have out grown the practice… Big up Maskal ndinu ma pioneers a modern music m`Malawi.

  5. Athumbi tatontholani mose mwayambira kulira muja. Munatha inu tangovomerezani basi. I know kunyoza anzanuku mukufuna attention ya anthu basi APA mwayipeza are u happy now???????

  6. Ukhalira yomweyo anzako akupanga makobidi.Iwe ndinyumba yomwe yosalongosoka mpanda wa tsekera kuvalanso kukuvute ntchito mowa basi,panga zoti udzasiyire ana ako.Zapa stage chikukukhudza ndichiani?Nyumba yomwe umakhala ingafanane ndi ya Maskal?Kuli Taygrin,Blasto,Theo Thomson ndi ena ambiri amayenda mma overseas ndikumakamenyanso bwino pa stage koma akabwira kuno samaloza chala artist aliyense kuti samadziwa kuimba pa stage.Iwe ngakhale ndi Makawa siungafanane kumbali yandalama but ur no.1 kunyoza anzako.Mowa weniweniwu umamwa kachasu mtengo wa black label siukuwudziwa.Udzafa ulindi mache…..okhaokha

  7. In as far as music is concerned …Maskal satha kuimba” ma off code.. plus pena ikwere zosakhala bwino”‘ i like his music thou'” koma satha kuimba & i dnt hate hm.. koma chilungamo

  8. kkkkkkkkkkkk chonchi tisamabene? kumangopanga zin2 ngati mugula nokha bwanji ? pangani zoti an2 akamva akodwe osati kuyambanitsa an2 omwe amakukondani!!

  9. ine ndichifukwa chake ndili Nganganga pansana pa #PIKSY…iwe Matumbi ndiye CHIDZUKULU cha #DZITSILU….bwanji osapanga zako??? kuimbaso siumatha kuyambila kalekale matama okhaokha,,,chimbale chilichonse utatuluse amakupanga feat anzako,,taona sopato ukuyamba zandale,ulimbikile kuti uzafanane ndi PIKSY N MASKO,,,,kaya amakumenya ndani panyimbo zako CHULE iwi,,kulira kokhakokha munthu ngati CHIMwana

  10. chi page nchopasula anthu, guys zifuseni kuti ndiliti lomwe chi page chonyasachi chinapangapo post nkhani zoyamikila munthu or za nzeru ? ndipanga unlike basi, bye bye

  11. Truth always hurt mkanakhala maskal ndikanavomereza past weakness coz 2mbi amakamba zanthawi yakale not now! kmaxo oyimbanu mumaziwana bwanji Lulu ndi 2mbi ?

  12. Nyakwawa amatha amwene …. mukufuna muziti chani apa inu zoti maskal amalowa ma off code nyimbo yokhala yake simunaziziwe…..samathadi pa stage Maskal ndi studio artist basi

    1. ma off eni eni…ine it was lyk i was joking nyimbo ya zilindiwe” was telling my frend kut koma ndie walowa ma off ..kkkk koma mzoona” dzimamuvuta

  13. Kukula konseko kuzipasa zina la chikazi….Kufuna kutchukira zina la nzanu.muthu wankulu koma kumalira munyimbo..hahahaha….zakoyo ndi wina winner…malo mozenga milandu uko kulimbana ndi madolo…ndalama zojambulira nyimbo zinachokera nthumba mwako?eee?…..prat…panga zako zikuthandize mwina uzafika pa Maskal….koma i doubt if u will….amatumbo….sorry amatumbi…

  14. Ngati Matumbi anayankhula choncho ndiye kuti iyenso nthito saiziwa. Matumbi nyimbo zake zonse amajambula Video ataledzera komanso amakonda kugwira pa lisani ngati akufuna akodze. Mwachidule tinene kuti akumana osatha okhaokha koma powayelekeza Maskal ndi dhilu.

  15. Si anzathu awawa ndi ma haters nooooooooooono , ndipatsire machine gun ratatatataaa, ndipatsire bazuka kweeeeeee phu, ndashuta. I like Atoht manje Majerasi.

  16. nothing wrong here nde thumbiyo amalawi munazolowera kuyamikila mbora basi here we go with leadership hardships…. munthu akazuzula mwapeza nkhani kupusa eti munya criticism is there forever

  17. ma guyz a 24 u suck n’ honestly i dont knw kti amakutuman nd ndan bt u jst confuse ppo,cant work on me though.ingoxekan ma studio anu bax agalu opanda michira inu.

  18. Nsanje, kaduka,nkwidzi, uchisilu uli thoooo mumtima why mkumapitaso mma nite xool kukaphunzila kenaka muzapangeko post mapositive stories kutero Malawi azatukuka osati izii even kuvaya kujoni vep ndizambiri kuno mumatinyasa zomadanisa anthuzi inuyo alesi osakonda ziko lanu lomwe

  19. SITICHEDWA KUYIWALA – By Melifa yao
    Padzana Mabanja anali kutha ati chifukwa wina anachezera panzere wogula mafuta a galimoto,
    Makono Mabanja akutha ati chifukwa wina akumachezera kotunga Madzi a pakhomo,
    Kafufuku naululula kuti Chipala chinatulutsa Amalume ankatiyang’anira nthawi yovuta mafuta,
    Mchipala chomwecho chinatulutsanso Amalume akutiyang’anira panthawi yovuta Madzi inoyi
    Tilimbe Amalawi, Mabvuto akadali, ntheradi anthuwa ndamodzi, angosiyana Silang’i (Slang).
    Onena nkumanena, Amalawi sachedwa kuyiwala!

    Tsano yatentha nkhani ya UNGA, mosasiyana ndi kutentha kwaku Jahena,
    Koma yayi, Mapulezidenti athu, ku UNGA ndiye kokaziziritsira kummero,
    Enawa kuwadzudzula kuti ku UNGA mwatenga khola la Mbuzi latunthu
    Iwo akubweza mokumbutsa, amvekere enanu padzana mmatengera makola a Nkhuku ku UNGA komweko,
    Nkhuku zake nazonso, Misoti yokhayokha, a Tambala makamaka akuda ali phee kulera wana pa Nyasaland,
    Nkumapitiriza amvekere, Amalawi sachedwa kuyiwala!

    Tichilimike posunga bwino nkhani zochitika Masiku ano,
    Zidzukulu zathu zisazawaphonye za a katswiri a amasiku ano,
    Palitu akatswiri oyenda mmalere,
    Palinsotu madolo ena akafuna kutsuka nkamwa ndiye kuti apanga kapinyolo,
    Pakuti iwo wawo, ndi ukadaulo wopanga ‘Chenji Golo’ ndalama za boma nkukhala zawo
    Nkhawa ili bii kuti angakhale mmodzimodzi manja awo ayamba kuvala maloko,
    Akuwerengera kuti posakhalitsa sikisi julaye izawatulutsa,
    Pakuti Amalawi sachedwa kuyiwala!

    Wati Zii Mpira wa Ntchemberembaye, pamene wina akunyadira kuti waja ankati ndichoke aja pano andiyiwala.
    Zisankho zayandikira za woyang’anira mpira wa miyendo, inde matchona akumati mpira wamapazi,
    Achulukirenji wofuna kuyang’anira, a Samvamgugu nkati okakamira mopanda Manyazi
    Tawafunsani za ndondomeko za makobidi mmene akhala akuyendera, amayankha thima lili zii,
    Ali ngati wafunsayo ndimmalawi, osandaula, sachedwakuyawala.

    1. sanamunyoze man,,,,amat wapanga improve hevy,,,,oz d@ kunyoza,,,?nde muli buzy kumunena mun2 ot sanalakwe nkomwe,,,,amakupusitsan awa amatembenuza nkhan nkumalemba zabodza,,,

  20. mmh malawi 24 ur somehow bringing confusion it was of yesterday of coz but matumbi was nt trying to bring shame kwa #maskal he was tryin to appriciate that there is a big change kwa maskal

  21. Guys nkhani zinazi musamangotithera nazo data iyaa!
    Pali nkhani yapa?
    Osamalemba zokhuza ulimi wa m’thilira ndi njala yavutayi bwanji…
    Moti u dont know kuti oyimba ndi pachibwanawe and amakhala akudziwana nde mpaka buzy ndi chi article ngati zenizeni??
    Tilembereni zogwira mtima osati udzu mukudzula apawu…

  22. koma mumasowa nkhani eti??? asaaaah ndamvera sizoti ndamva kwa munthu he said poyamba maskal pa stage zimamuvuta but now anajayira amamenya bho bho amasangalasaso anthu…..muzitipasa nkhani zoti tidzitolapo kanthu osati za ziiiiii ngati iziiii asaaaah

    1. don’t say like that dear!!! news iyi imayesetsa Ku tipanga update nkhani za booh independently that’s core of peoffesional journalism

    2. but this news is out of truck…cnt u get it????? amapanga update nkhani za bhooo eya then why this instead of za bhoo wo zo???

  23. This article doesn’t make any sense. Try next time to learn how to balance a story,,,you are using ‘dresses down’ language and yet you fail to hear from Mascal’s reaction? Its like you are being in Mascal’s shoes..Poor reporter

  24. I understand he doesn’t perform so goon during live shows,but #Maskal is the best.. Annie Matumbi has to be taught how to respect other artists works as an artist ?.. Osati kuyakhula pa TV ? show kuti Maskal Samatha,iwe ndiye umatha????? Poti nyimbo zako timaxikonda coz we like ? you not your music… Instead of encouraging your friends ukumawanyoza….. #Zooooooooobbbbbbbbaaaa!!!!!

    1. he said maskal wachita improve oz d@ kumunyoza man,,,?mukngotha zankamwa chonsecho smunamvetsetse zomwe amanena,,,,komabe maskal nd zoba wakulila muja kmapala pastage,,

  25. wen u got paper n u pai 4 toz xpensv studioz doznt min u gwd!………ts not anly him hu hu forcd music in hiz o he path!..includin matumbi yoxo!…. oxamangogwra mu officmo bwnj!

  26. Thats true Maskal aint Musician I got Dissapointed when i listened to his song Called “Ndiwe Wanga” the Lyrics are wack he goes like “Chikondi Chathu akuziwa ndimboni nkona sinalakelake zopita ku Joni/chikondi changa sichapa phone mkona sinapite ku Bank kotenga Loan/” whats that?? There Is no connection Of Words there at Kaya Rymming eni akewo Mxiew it sucks

  27. anthu osatha kuimba ndi choncho ka amalimbana ndi anzawo..nyimbo ya kape ameneyu kuyamba mpaka kutha kumangolilamo..wat a phoney

  28. Are you bringing unity among Malawians or divisions among people. Media is there to bring good report to the listeners and readers. Have you called Matumbi and ask him why if he real true that he commented so? The first thing before you write, you need to ask from both parties and have a concrete truth and then you write your article. Thereafter your Chief Editor if you have, must check and sign that the public should read. What you are giving to people are lies and nonsense! Stop this before you are put to the Book of Law!

    1. thas true!thse r irresponsble mediahouse described by the presedent….giving people incoplete&uninvestgativ stories…nice co.

Comments are closed.