Mapemphero anasokonekera ku Lunzu wansembe atathira bakera kwaya masitala
Zachitikanso lero mumpingo wakatolika ku Lunzu pamene wansembe wathira bakera kukamwa oyambitsa kwaya kamba koyambitsa nyimbo ya Aleluya mu nyengo ino ya lenti mpaka mapemphero kusokonekera. Nkhani yonse ikuti a Edward omwe ndi oyambitsa kwaya… ...