Japan yapereka ndalama zoposa 1.99 biliyoni ku dziko la Malawi
Dziko la Japan lapereka ndalama zoposa 1.99 biliyoni kwacha kudziko la Malawi kudzera ku bungwe la UNICEF kuti zithandizire kuthana ndi ena mwamavuto omwe alipo m'madera ena omwe anakhudzidwa ndi Namondwe wa Freddy. Malinga ndi… ...