Wamwalira pampikisano wazidakwa atagugudiza matoti 42 a kachasu
Bambo wina wazaka 49 wa m’mudzi mwa Binya kwa mfumu yaikulu Kwataine ku Ntcheu, watsikira kulichete atamwa matoti 42 akachasu pampikisano wazidakwa opapira bibida omwe unachitika dzulo mbomali. Nkhani yonse ikuti dzulo lolemba pa 11… ...