Amwene, ndapita – Mwenifumbo watuluka UTM

Advertisement
Almost a year after quitting the UTM, revelations are now rife that politician Frank Mwenifumbo—who after being in the Democratic Progressive Party (DPP) returned to Alliance for Democracy (Aford)—is forming his own National Democratic Party whose funding is allegedly said to be sourced from South Africa.

Watsatira Winiko, naye kudzisiya. Amene anali mneneri wa chipani cha UTM, a Frank Mwenifumbo, atsanzika kwa mtsogoleri wa chipanichi, a Saulos Chilima.

Malinga ndi chikalata chimene Malawi24 yaona, a Mwenifumbo ati iwo atula pansi udindo wawo ndinso atuluka chipani cha mu boma cha UTM.

“Ndaona kuti ndikapange zina, ndayamba ndapuma ku ndale,” alemba motelo a Mwenifumbo.

Iwo ati akhala akufuna kutsanzika koma amalephera kamba koti Mayi Chilima akhala asakupeza bwino. Tsopano, iwo ati basi aona kuti ndi bwino alondole msana wa njira.

A Mwenifumbo achoka pamene zikuoneka kuti ubale wa chipani cha UTM ndi MCP suli bwino konse.

Advertisement