Nkhanza za Chakwera zandipititsa ku DPP – Jumbe

Advertisement
Felix-Jumbe

Wazitaya. Wazinyanyala. Wazidomoka. Wayendela yake. Wapita atanyangala ndipo walalika kuti a Chakwera ndi munthu wa nkhanza asananyamuke.

Phungu wa dera lapakati mu boma la Salima a Felix Jumbe alengeza kuti tsopano alowa chipani cholamula cha DPP.

Felix-Jumbe
a Jumbe alowa chipani cha DPP

A Jumbe alengeza izi kudzela pa tsamba lawo la Facebook kuti tsopano iwo ndi a chipani cholamula ndipo mu 2019, iwo akuima ngati wa DPP.

A Jumbe anenanso kuti iwo sazaimanso ku dera lawo lapano, ati m’malo mwake akukayima ku dera la kumpoto mu boma la Salima lomwelo komwe kuli kwa Mayi awo.

Atauzidwa kuti iwo akagonja kumene akupitako kamba koti DPP ilibe chikoka, a Jumbe adanena kuti anthu ndiwo awatuma.

A Jumbe adachotsedwa mu chipani cha Kongeresi mu chaka cha 2016.

Ngakhale adatenga chiletso ku bwalo la milandu, a Jumbe ndi Kongeresi akhalila kulumana.

 

Advertisement

172 Comments

  1. What agood and mature decision you have made.Ndipemphe anzanga aDPP.Mulandileni ndi mtima onse nzanuyo.He is intelligent young man.He can help the party do good things in addition to what you are already doing.I don’t hate MCP.Its where we are all coming from but we need true representation in the party .Not power on type of leadership but power to.Muwuzeni Dr. Kabwila aganize bwino naye.Tikusowa nzeru zake kuyendetsa dziko.Akapusa akhala garu wa Mbusa Chakwera.Uladi Mussa;You are intelligent make a quick decision before its too late.Late make Salima home of peace and wise politician.Ndakulila mu MCP ndikudziwa chomwe ndikunena.Ndinakhala Earial Treasure ndili Std8.Iwas forced to and Idid what they asked me to.I love the party (MCP) except what I see and hear.Good lucky Jumbe.

  2. Its a bit late,go and finish yourself that side,here we don’t worship idols I can clearly c ur downfall

  3. kumangoomberam’manja ndizitsiruzomwe ngatiJumbeyo aDPP mukusowaanthu? tifuseni ife akuSalima Central, tikuuzenizagaluyo

  4. Pepani pitani bwino osaononga dzina lanu.We need true leaders.Chipani sichamunthu amodzi.Achinyamata alowapo mwachokapo.Ndale zabwino Malawi wabwino.But Ku DPP akusalani achimwene!!!

  5. Mbava zakumalawi ntchito kuba ndalama yamalawi,inu ajumbe muzakhutisidwa lit popeza anthu nonse okuba muli pafupi ndi zenje lamantha.muona mulungu akukhandani.

  6. Love it, hate it. It’s still a gain to DPP. Can MCP tackle the 50+1 electoral reforms? Definitely no. Slowly its bargaining power is reducing on the electorate.

  7. Zabwino zonse bwana…….koma muzisiya phazi osasiya mulomo. Dzikoli kapena moyowu uli ngati pelete Wa asilikali. Imafika nthawi ya about turn!!!!!!!!

  8. Chosangalasa apa ndichoti amene amamuika pampando wa uphungu alibe ngakhale foni ya watsup ,Facebook ,ndipo ubwino wina ngoti amakhala kumudzi inu amene mukumulandira jumbe musaiwale enanu ndinu akumwera za consti ya kusalima simukuidziwa .
    Madera anuwo mukadakhala kuti mukulandirayu mudzavotera so 2019 zikadakhala bwino ndithu .
    Ngati mukukumbukira DPP mudera lomweri kudali candidate wawo amene anaimira chipani cha DPP ndipo anthu ngakhale amkadziwa kuti DPP idali m boma bingu asadamwalire adasankha a jumbe sichifukwa cha mbiri ya chipani cha MCP koma kuti anthuwo amakonda MCP mmoyo wawo monga anthu ena so amakondera DPP komaso UDF tsopano inu amene mukuwalandira awa mudziwe kuti anthu amene adawasankha a jumbe sadasinthe ai ndiomwewo .
    Monga ku dera lomwe amkaimira a Gwengwe chaka cha 2014 iwo adapita ku PP koma anthuwo sadapite ku chipanicho .
    Enafe ndale sitizidziwa timangoona chomcho anthu ngati ife tisamakonde kunyoza zipani chifukwa mawa tingadzakhumudwe

  9. Apite munthu uja amadana naye heavy.Amakhala because of Court rule. I think congress will never complain about it.

  10. Alibe zolakhula uyu nanga constituency imene akuithawayo kumati akaimira kwina kuliso khadza? Ndiwosakhazikika uyu komaso palibe chomwe amanga chooneka.

  11. Mr Jumbe,, Lucious Banda Anayimba nyimbo yoti” anthu ena akuyenda ndi themberero la makolo awo, kumtundu kwao,kuwathandiza umangotengerapo tsoka ”

    Mcp ineyo ndimkayiopa with combination of Juliana Lunguzi, Chakwantha, Jessey Kabwira, Felix Jumbe,,, u guys u really made mcp to shine to higher levels. However alipo ena mchipani Amatenga kuti mcp ndi ya ku lilongwe, munda wa ambwiyao they dont want change…

    U are our next minister of Agriculture..
    How Iwish Juliana, Jessey could join u… ikanakhala sweeping ya Eastern part of lilongwe,, Dedza East, Salima yonse, remember Uladi Mussa, kjkkkkk u pple u pple…. Congratulations!

    1. You can say that again & again no one can throw you m’damu la ng’ona.Congolese nthawi yawo idapita. Madzi akatayika saoleka,lero likapita tsilibwelera.

    2. Koma chipani cha MCP ndichotchuka zedi.tsiku silitha athu osatchula oti cadet sakumvesesa kuti nkholokolo zipite

    3. OIPA amathawa yekha and the same as of David and his son Absalom,,, zidamuonekera yekha!!!!kodi majority ndi imene imanena ubwino wa munthu than empty teen as he is!!!!amene uja ndi kadawe,nkholokolo,,,ndiye leave Chakwera alone,,,,ma political heavyweight alipo,,,oti kubweretsa anthu ambiri, and ma recycled politicians ndamene akupangitsa dzikoli kusapita patsogolo,,,amati pamene waimapo usachoke ,,,,osati uku wapita ukuso wapita,,,sumayanga ndere,,,anthu ake amakapanga apply zomwe ankachita mu ulamuliro wina kupititsa Ku chipani China China,anvekere APA sitinkatere,APA pamakhala choncho,,,,opanda chosintha,,,,mbuzi zokhazokha,,,,that’s why nkhanza ankachita Achina dausi ntaba, azilikobe Ku DPP,,,,Iwo ndi amene adali oipa,and MCP kuli anthu okhazikika and moreover focused, osayendayenda,,plus more new blood,, mindsets and leadership,,,, nthano zanuzo ife kudalibe,if tikuona nkhanza zilipo panopa not as of 70-80s we in 2000s dzukani,,,magogowa atibera mokwana,,

    4. Ndikudziwa kt anthu achigawo chapakati zimakunyasani coz nyau panopa zilibeso mphavu akuti ugule njira ndwe ndani ndye mukufunaso muzigwila nkhuku za wanthu mbuzi inu kumtima kwanu mbee kkkkkk kuli chance chimenechi kumwela kuli anthu ochuluka mokuti only two district DPP wayina kale ine sindipanga nao zandale bt u must for get kuti mudzawina mwana nkulu akudziwa zambiri ya chipani ichi cha MCP zitchito sake no matter mukuti chani chani fisi ndi fisi sangakhale mbuzi or atasitha mawanga kkkkkk kuli kanthu kokanthula ndi chala uzalakalaka kulowa pasi

    5. OWEN ngalande,,, nyau sizoseweretsa and nyau zilibe chipani zimapita pa msonkhano wina uliwonse,osati zopusa ukulemba apazi,,,, nyau ndi gule wa achewafe and zomaphatikiza chikhalidwe ndi za ndale,, muvulalanazo,, achewa amacheza,kapena nditi kulodza,,,,,,kawafunsa a sheikh a kumitundu zomwe adaziona,, ambiri zodawachitikira!!!!ndiye samala ndisadzakuveso ukulemba zopusa ngati zmenez and wati sii iwe wa ndale,why wanena za DPP itha kuwina in 2districts,, ndizo ndalezo komaso za regionalism,,,,, zinazo ndi chabe,, koma nkhani ili APA, pa nyau!!!!!!

  12. Uli dere nkulinga utayenda naye…Che Jumbe are you serious? Ndiye muthakotu coz we need a consolidated opposition.

  13. KKKKKK ndiye anthu akudela lakwanuwo uzikawauza chani? Mesa munkawauza kuti DPP ndiyakuba ndiyopanda chitukuko ndiye lero udzikati chani Jumbe? KKKKKK akulu mongofuna kukutsimikizilani munene kuti Dyela langa landipititsa kumbava zinzanga mwamva, mwachitanso bwino mwina mukaba muwathandizeko abale anu aja Ku mchenekaku, munthu osakonda abale ako ngati iwe ndiye ndinali ndisanamhoneko, koma zomati nkhaza za Chakwela xandipititsa Ku DPP aaaah udzikauza Ana ako ndamene umawaimilawo kumunda kwakoko kusalimako. Enafe ndiye sitinfamve ndipo ukunama kwambiri. Zitaye zokamba xopusa zakozo munthu wadyela ndiogulisa ufulu wako iweee. Kadyeni ndimbava zinzakozo .

  14. Should we still believe to say leaders are being chosen by God Almighty if so why all this mess in our country? I guess we don’t have leaders but rulers who are directly appointed by serpent just to destroy this nation. Let’s wait and see

    1. Yes every leader is Shosen by God but the purpose is what matters. Sometimes God brings a person to teach something. Good or bad. We blamed muluzi for the rain which didn’t come but things were much better that time.

  15. Ngati Palimunthu Oti Amabwelesa Phokoso Mu Mcp Ndiameneu, Mwachita Bwino Kuchoka Pitani Akakuweteni Ena.

  16. Jumbe akanati Chakwela ndiwopenya patali anandidziwa kale kuti ndine kavue vue ndiye anandithamangitsa ine ndikanamva koma waona kuti zomwe amatumidwa ndi agalu a dpp sizitheka ndiye wathawa yekha

  17. zomwe umapanga ku mcp upangeso kumeneko tione ngati angakusekerere.ife timaziwa ndiwe wa dpp koma unkakana

  18. Political career yathera pomwepo, kafunse Kalebe ndi Kutsaira, Gwengwe anatsala pang’ono kugweramo mwai wabwelera.

  19. Timanena life kuti Yona simunthu. Ndipo sanati chifukwa anthu anakamuthawabe. Atsalamo yekha mmenemo. Munthuyu ndi dictator, samba zamunthu. Kukhala president wadziko tidzazunzika kwabasi.

  20. Mutayen waona ndalama akugawanazo, anthu oononga dziko awa. Nawoso anthu aku Salima muziona anthu owapatsa vote, munthu wadyera ngati ameneyu? Wachita bwino tionana miyezi ikubwelayi

  21. Akunama ameneyo ndikazitape MCP moto kut buuuu asafuna asiye ndivotera MCP yomweyo ng’ombo zichedwan ndizanuzo

  22. He dont have a name in politics let him go back to farming. He is a good farmer and we admire him for that

    1. this is your end my friend DPP just put people down watha basi you will never again win on mp seat ;;;;;l know people of central region they vote for party which MCP not aperson you have end

  23. Ndichifukwa chazisilu Ngati ziachina jumbezo Malawi ili yosaukabe they cant stand a real man like Chakwera.

  24. DPP must not allow this oppotunist Jumbe an automatic entrance into the party system coz he a spy he need to break the party from within pliz be carefull of Chakwera spys

  25. He knows his political career is as good as over so at the moment he has to maximise chances of accumulating wealth through association with DPP before the next elections. Basically he doesnt give a damn what.happens in 2019 so long as he is rewarded now…

  26. Chomwe chimabvuta kwa anthu amene amabwera pa zochitika zina zili zonse ndi cholinga chofuna utsogoleri wa ukulu pa gulu ndipo mkupezeka kuti zomwe amafunazo sizinatheke amakanika kuchoka mwaulemu kuti mwina komwe akupitako akalandilidwenso mwa Ulemu sindikudabwa ndi jumbe maka machokedwe ake opita akutukwana paja amkabwela ku ndale pofuna utsogoleri chimodzi modzi cris Daza anthu ngati awa ndi ambiri koma chomwe amayiwala ndi chakuti Pochoka udzisiya phazi mulomo umakutsata !!!!!!!!! Bwanji osamangopita ku dimba kuja amalima tomato kuja???? Chifukwa alowerako mmmmmmmmm kaya poti ndidawonanso kuti anthu akusalima amangotolera ndi sakalasi zomwe kumati ndadinda ma belo khumi afodya kumeneku kuli iyeyu #jumbe #kabwila #oladi_musa sindidziwa kuti kapena poti amati mbewa zikatha anona ndi swiswili!!!!!!!!!!

  27. Palibe chake sanga wineso uyu ndimwayi chabe ku wina komaso sitikumudziwa mdela lathu uyu and pano tinapezekale wina m’dera lathu oyimila awa kwao kwatha

  28. Oipa athawa yekha
    ameneyu asaganize kuti adzabweleraso ku nyumba ya Malamuro pakutengelaso komwe walowelako
    palibe phungu wachipani china yemwe adapambanako ku Salima north kumeneko kuli Kamphantengo Yona amene kugonja sakudziwa ndiye awa musiyeni awona polekela sangawine ngakhale zitavuta motani Salima north ndiya Mcp basi

  29. jumbe nde zitinso?zimaoneka bwanji?ndingazipeze mu Shoprite kapena mwamavendor?mwina galu wanga angazikonde

    1. Mulipo ambiri koma simungapose a DPP. Nde pajatu 50+1 inakukanikani,mukuonapo tsogolo. Mukhala kotsutsa mpaka Yesu atabwera.

  30. Come here in RSA and learn how democracy is, where the know how to remove a president from his seat if he is doing kak stuff, there you will just sing asong

  31. Wachita bwno kuchitaya chipani cha uchikepe MCP iwe jumbe mbuzi singabale galu ayi ndye nkhaza awa ndizoyamwila wapanga chisago chabwino kusangalasa mtima wako not makape ankhaza magazi adakalipobe manja mwao kkkkkk anapha a gadama ,amatenje ndiomwewatu mwaiwala ndiye malawi wachilukano akufuna apheso anthu

    1. Adapha agadama ndi Mtaba, Adausi ndi a jumbe lero onsewa alikuti This is New mcp baba oyipa akuthawa yekha man

    2. Eee,meaning ya Nkhanza ndiyochitsa anthu mu chipani osafuna kumva mbali yawo Ndizomweso munkachita nthawi ya kaMuzu . Nde ubwino wake simudzalamuliraso. Tangoganiza iweyo,DPP inawina ili ku opposition, nde kuli bwanji ili mkati. Tiye nazoni,bola osadximangilira chaka cha mawa.

    3. Ngati MCP ikhoza kulemphera ndiyekuti ibera Nkhanga tango ganiza kuti zisankho zapedera DPP palibe mpando umodzi chidaeinako ndiye musanamize athu muthu wanuyo tengani tikufuna kuti chikhale chantendere osati umakhalira ukangana ena akubwera kaliwo kabwira msowoya.

    4. Galu wa chabe chabe ameneyo Nkholokolo ayende bwino wapita kwa amzake akuba kumeneko ndikomwe akuyenela kukhalako

    1. Sanamwalire,anakomoka pomuza kuti malo one azaza,VP pali chilima,atupele ndi msaka,bwana akusowa kusankha

  32. I love politics coz amakhala zitsiru ndi amene amavotera mp yo anthuni kunjinjilika kungosiya munthu pa mpando inuyo kumavutika ufulu wake uti pamenepa simunamphuzilebe ine ndie ndinasiya kupanga zopusazo

  33. Mutsazikiretu anzanu ku parliament chifukwa kuno ku Salima Central simudzawina sitikufunani ku constituency kwanu mukuthawako zichani.Muyende bwino

  34. who dont know felix jumbe that is the one who brought terible and complicated stuation to mighty mcp?is it, there are some people who are lacking jumbe^s downfall information from our party?the fact is that jumbe uprooted himself after being rejecting the plans of Dr Chakwera to bring reforms of tackle every region and give them shine responsibilities, he wanted to ocupy all of these himself which is not good thing withought dought he will never win the elections bet!

  35. Thumbs up !! jumbe. u dont want to sit on the opposition benches next year kkkk, poti congeresi ndi opposition anachita kupalana ubale waukazembe kkkkkkkk

  36. Aaaa iwe jumbe usatinyasepo wanva,azakuziwa ndani kuti inu andale ndizomwe mupanga mwinaso nawe uli gulu omwe lapasidwa ma 40 million chosecho anthu akuvutika.wawona kuti nthawi sili ku mbali yako wati ukabeko ku boma.kkkk ndale zanu nzosapindula ku dziko tiwonana 2019

  37. Wanyansa lero?? Kkkk koma a mcp mumandisangalasa mwamva. Mbalame ikathawa mumvekere kunyunya msuzi iwe olo nkanakupja sindikanakutola. Kkkkkk ndale nkanyama koipa mungofasa muziziwe ndale kut nchani? Si munkangobwebweta pa fb? Zangoyamba mudziwanso kut dpp si masanje ai. Ndale sitisokosa. Ndale sitiyima pa chulu nkumati ife ife ife ife. Ena amangofasa nkumangoyang.ana koma akupanga ndale za pansi
    Koma neba suihawa? Neba suihiya? Neba hauthawa?? Neba ndi imeneyotu

    1. Ameneyu aiwale za kunyumba ya malamuro mmene ndili kuidziwila ineyo Salima north mmmmm wakula watha aziona

  38. Munthu akasowa chokamba nichoncho,, nothing can change MCP,, azipita akapitilize kuba ni mbava zimzake ku DPP ko, & l’m still MCP member mpaka kale kale

  39. Zisiyeni tiligu ndi namsongole zikulire pamodzi zidzaoneka pokolola…. BACK TO THE SENDER…GO IN PEACE KUTI MCP IKHAZIKIKE

  40. Nkhururu Yachabe Chabe Imenewo Amaoneka Ngat Wa Mcp Km Al Wa Dpp Wakhoza Stingadande Amasokoneza Ameneyo

  41. Achatabwino kwambiri koma chimene angaziwe ndichoti 2019 ayiwale zoti akalowanso mu august house. He’s a confusionist.

  42. Tsogolo lanu la ndale lathera pamenepa ankolo. Mpaka kuthawa komwe inu mudaimaira poyambirila. Aliyese sangachite kufusa kuti oipa ndindani. Abambo inu ndinu oipa zedi. Mumafuna kuti mutiyipitsire chipani chathu

  43. Linda madzi apite ndiye uziti ndadala, ukamachoka usasiye mulomo…….ku Dpp kuli kuba

Comments are closed.