A Malawi oposa zana athamangitsidwa ku Sasafulika: ambiri ndi a ku Mangochi ndi ku Mzimba

Advertisement

Abwelako ku Joni opanda kanthu. Angobwela ndi zovala zapathupi pawo ndi kaselula basi. Kaya ayambila pati kumudzi kuno?

A Malawi okwana zana limodzi ndi theka kudza mphambu imodzi (151) afika m’dziko muno atathamangitsidwa ku South Africa komwe amakhala opanda chilolezo.

A Malawi awa afika Lolemba pa 29 kudzela pa bwalo la ndege la Kamuzu International mu mzinda wa Lilongwe.

Malinga ndi mneneri wa bwalo la ndege la Kamuzu International, a Martin Gondolo, abambo okwana 149 ndi amayi awiri ndiwo anafika m’dziko muno atatopa ndi kukhala pa malo a Lindera podikila kubwela kumudzi.

Umboni umene tapeza a Malawi24 waonetsa kuti pa a Malawi omwe afika m’dziko muno, ochuluka akuchokela mu boma la Mangochi ndipo kenako Mzimba.

Pa a Malawi 151, 62 ndi ochokela mu boma la Mangochi, 41 ndi a ku Mzimba, 5 ndi a mu Blantyre, 11 a ku Machinga, 7 kuchoka ku Nkhatabay, 4 ku Dedza, 7 ku Mulanje, 5 ku Chiradzulu, 8 ku Zomba and mmodzi wa ku Nsanje.

Chaka chatha mu mwezi wa December a Malawi ena 72 anafika mu dziko muno atathamangitsidwa mu dziko la Zimbabwe kamba kokhala opanda chilolezo.

 

Advertisement

152 Comments

  1. Tibwelerakoso ku South Africa without passport and pay forward alright…ndikwathu kumene kuja, mwana mamuna ndi Kabudula athera moyenda.

  2. Kma walembawe umaganiza??? aaaaaaa sionse olemba nkhani ali oganiza bwino oyamba ndi mbuzi Iweyo. Zoona mkumafusadi kuti ayambira pati? Iweyo unayambira pati kuti ufike pomwe ulipo?? Kayimbi Iwe xweeeeeee

  3. Deportation siinayambe lero, timagwidwa nkupitanso ndipo sitidzasiya kupita. Kusiya kwake Joniyo ikafika poti yanyenyeka ngat Malawi ino mpamene tizasiyire, ndipo ndikuuzeni ife monga Ayao Dera or Dziko lomwe lituluse fungo la Ulemelero/Chumalo tilikomko. Mwamuna azikhala olimba mtima. Zokhoma mwaife zinatilowa mmagazi. Ndipo kugwidwa munthu sikutanthauza kuti alibe chilichonse anthu amagwidwa akupita kuntcito or ku shop, zomwe amakhala nazo panthawiyo zovala za pathupi ndi fon mmanja katundu amakhala alikunyumba ndiye (DEPORT) imeneyo. Kusayenda nkumene kukuyankhulitsani mbwelera baba

  4. The first thing is that all the pensioners should vacate the office and give room to fresh young bloods, second we should stop employing old people as presidents as we have seen that they dont have the welfare of young people at heart.

  5. Anthu onse ali Mboma ndi mbuzi za anthu saziwa chomwe amachita.Ngakhale mutawafunsa lero mwachitako chiyani chothandidza anthu dziko muno? Yakho 2019

  6. Katundu wawo ndi Dora tawasungila kuno.Timangodikira kuti tomve zoti afika kuti tiwatumizire.Iwe udera Nazi nkhawa ndiabale ako,kukamwa kobwafukako selk

  7. Inu a Malawi 24 tamalembani nkhani zeni zeni ndithu, kodi inu mukadalibe ndi bodza polemba nkhani zanu m’pakana lero lino?? Chomwe mungadziwe inu nachi :anthu mukuwanenawo adamangatu nyumba zawo m’makhomo kwawo ndiponso enawo ali ndi ndalama kumudzi kwawo tero ilo sivuto ndipo chifukwa choti adadzolowera kugwira ndalama mawali abwereranso ku South Africa ko.Iwo sianrhu wamba ai ndipo inu a Malawi 24 ndiomwe inuyo mukuwaona ngati ndi amphawi koma sichocho ai ndithu ndipo atsatireni kwawo mudzachita manyazi nokha ndi bodza lanulo ndithu.

  8. Ineyo ndinava kuwawa zitandichitikila zimenezi ndiye iwe ukuyakhula mopusa mboleyako ndipo ukanandiyandikila ndikanakupha phwalalako iiiiiii iweeee oky

  9. Sikoyamba kugwidwa anthu deportee zidayamba agogo a agogo ako asadabadwe sizachilendo izi..and it’s not only malawians wh r being deported from RSA and its not only in RSA wher they are deporting illegal immigrants
    ..and its not a strange situation kuti munthu akagwidwa deportee amapita opanda kanthu kumudzi..and this doesnt mean kuti pamene agwidwa awadula miyendo ndi manja kuti asadzabwerenso ayi..
    Try to bring something tangible here rather than bringing parasites of stories

  10. My Jesus Malawi its a long way from South Africa its so painful to return home without even a capital to start even a small project.lm a Zimbabwean but l once felt shame when l was in Brandfort near Bloemfontein l saw a Malawian man he was mad,l even ask myself,WHO IS GOING TELL HIS RELATIVES THAT HE IS HERE AND HE IS MAD.even to ask anything nothing was able to come out.l wish if they deported that one not these ones.

  11. mukamalemba zinthu mumalemba mopusa ngat inu nde muli ndi kanthu bwanji lembani zot tikawerenga tizimva bwino not manyi anu mumalembawa

  12. Kkkkkkkkkkkk koma iwe ndiwe wa phuzo yeti athandize kaya ndimayesa ndi azibale ako amenewa apase chochita mawa azathandizaso iwe

  13. Home boys pa mangochi sipamavutakubwelela ku joni mayazi ndipo sikuyamba kubwelela chotelo come back guyz dnt worry things happen worry nt

  14. Ife siaulesi and I agree with you Elias M. Pemba. Ngati pali mtundu wa anthu amene saopa kupita kwina kulikonse ndife a Yao. We always get what we wants and that’s how it works. By the way, ife timayamika Mulungu chifukwa tayenda ndipo tadziwa mabvuto mmene amakhalira unlike ena mwainu munabadwila ku CheMusa and grew up in Likoma. Koma ife kuno ku Joni takumana ndi mazangazime but that’s how it is. Ambirife simbuli so you should know. Tili ndizinthu zazikulu zikulu zomwe tapanga because of the you call it; sasafulika in your version.

  15. Adapitila ndalama zawo abwela they know how to source money iwe phee umaona ngat they hv nothing in store.empty tins shame kwa mlembi wa nkhaniyi udzafa osauka

  16. Mwaonatu bro.nyaupe uja mnatuma admin kuti adzigulisa wayamba kusuta yekha.chifukwa chake akuleba zoduka mutuzi

  17. Ndipo ngati afika awuzeni kuti adzibwebwera olo pay forward sibvuto akwele kunyasalande ndi dziko lokhalo lozuza anthu inuyo ngati mukukhalako mumangokhalira bola moyo emweyu masiku mkumatha mpaka kukalamba

  18. abweleranso komweko si nzika za Malawi nzika zimakhala ndi ma national Ide ndiye akaponyedwe ku dzaleka ndi ma refugee amenewo

  19. Walemba nkhaniyi ndi bakha weniwen omwa pa chithaphwiiii……ndipo Ku utolankhaniko u never fully qualified unangogula ….
    Rubbish reporting…

  20. Anyapapi akuti anthu omwe amachoka dziko lawo kupita maiko aweni ndi alesi. mukamva umbuli ndi umenewo kuyambila iwe amene walemba nkhaniyi ndiwe kape. amene mukuti alesiwo kukhala kumeneko simungawathandize munjila iliyonse ngati likulephela kukuthanduzani boma.ANYAPAPI ndalama yomwe anthu akulandila patsiku Ku SA inu ambili mukuthoka shit pamwezi simumayifika pan…..yo…..pa…..nu

  21. I like these guys I call them the dreamers wosamadandala kuti zinthu pa Malawi sizikuyenda kumachangamuka kumapita malo wopezeka zomwe tikufunazo basi

  22. Musaiwale kuti amadyesa akhwangwala osalima what more munthu wanyonga zake? May almighty God be with you guys.

  23. Tiwarandire tiwarandire tiwarandiree
    arendo athuu tiwarandireee abwera lero tiwarandireee!
    pano siyinuso Makwerekwere mwava?

  24. Welcome back to Malawi.East west home is best and thank God that your still alive guys.Don’t try to go back again to SA but seeing way forward for saviour. Our God we save is in control of everything.Your past gonna be a history and this challenge for reading survive gonna mek u grow

  25. Welcome back to the paradise but full of parasites…………… Nkhuku zotchipisisa zija mudzisowaso, ma baby otchipa aja kuno sapedzeka, mowa osamba uja kuno mudzijiba kwinako muona kuti mutani…….. kunoso kuli K2000 yapepala

  26. Koma na amalawi, mwenzi wose uno tidzingomvatu yokha yokhai, basi. muliuze boma kuti afikapo amapatsidwe ntchito kuti asabweleleso. chifukwa afikapo ena afikakale kutheba ena akukonza zobwelelaso.

  27. TO FRIENDS AND FAMILY I JUST WANT TO ASSURE YOU THAT I’M STILL LINGERING AROUND IN SOUTHAFRICA GOD IS IN CONTROL!!!.WHEN TIME COME I WILL LET YOU KNOW BUT AS OF NOW I’M SOUND AND SAFE!!.

  28. Iweyo ungopita akakugulitse phone yakeyo, chifukwa iwe ndi amene ulindi anthu oti uziwayimbira. Iyeyo m’mene anali ku southafrica, unamva kuti anathetsa ubale ndi anzake? Kulankhula mopusa, iweyonso ndimodzi mwa anthu ogula katundu mwakuba.

  29. Chonde potipatsira nkhani mukuonjezatu pena kumamvako chisoni vuto ndi ulova,,, nanga sikuti boma lathu likulephera ku walemba ntchito achinyamatawa…ngakhale paonkha angathenso kuzilemba ntchito…Tamva

  30. Deal imeneyi ndikunziwa amene waipanga push siwina koma AKA hash tag Pitalaaaa.Cholinga fans ipangitse ma ID opanga expire anga ndi bread.The more I know Madolo omwe apangidwa deportee-wa abwelera ASAP deal imeneyo ikanika.

  31. Zoziyamba dala, sindingawamvere chisoni ine..kulowa dziko la eni popanda ma documents or kuphedwa zimathekanso coz u threaten the security of the country.. Ife tikadalima kuno, mvula kuvuta koma kangachepe tikolola ndithudi nkumadya masiku nkumavaya basi.thank God u r back alive..paja ma guys APA South Africa amaotcha akafuna….phee in Malawi ife

    1. komwe samaotcha ndikuti,komwe amampha anthu osalakwa kumati ndi anamupopa magazi ndikuti,?aliyese ali podalila inu zilimani,akupemphani ndalama yama documents mukufunawo?komaso sizinayambe lelo zimenezo.tazingoyamikani satana wanu kapena mulungu wanu kuti mukolola.sanakupemphe chisoni chako ali kale ndabale koma mabwezi awo owamvela chisoni osati sayenda iwe.umbuli osaona malo ndimayiko ndichocho.

    2. Kulankhula kopusa,sitisiya kupitabe,next wk tili komko,iwe uli chikhalire kumalawi ukuganiza ungafanane ndi amene akuyendawo

    3. Ada inunso NDE kayatu….
      Udziyenda udzaona ndi kudzikindikira cifukwa chimene anthu amachokera ku MW kupita Ku SA….ndipo udzamvetsa kuti sikungofuna kusiyana ndi abale awo okondedwa kumudziko ayi koma kamba ka mavuto …anthu amakasaka kuti mwina nkukhala odzidalira atalephera kuyesa yesa kumudziko zinthu osayenda….
      Komanso udzamvetsa kuti Ku Joni obwera si a Malawi okha a Ku Mzimba kapena MH…kulinso Nigerians; Congolese; Somalians; Ma Taifa; Zimbabweans nde kwao ….
      Osamafulumira kulalata poti ndi pagulu anthu akuchemeleleni chosecho mukulankhura zoti simunadzionepo ndi kudzipanga experience.

    4. Sindingapite ku joni nkumakayenda mozemba mudzina losaka ndalama…zaziii…kangachepe ndimapeza kuno kamakwana wamva Andre? So don’t think ndidzasirirako mapitidwe ake amenewo, NO..xenophobia mwaiwala kale alunji? Sanapemphe chisoni changa yes, ngat mmenenso ine sindinalemphere timaganizo tako pa comment yanga..ukagwere kutali mwana waulesi iwe… Aaaa hasan opusa kwambiri ndinu, mmalo mongolemba comment yanu explaining your feeling and altitude muli busy kupanga za comment yanga, nde kupusako kumeneko..ngati ndikuganiza mopepera osangosiya inuyo nkulemba zanu zanzeru zopotokazo bwanji…i can’t support za ku SA or mutandilozetsa mfuti mmutu..dzipitani mudzikabwerakonso opanda kanthu, tikaone kuti udolo wake ndi uti……ndikudikira chitsitu china chopanda nzeru chiyankhenso mwaugalu mmalo mongolemba maganizo ake pa comment box…mxiewwww

  32. Kod fans mumakonda kulimbana ndi fan’s ya jon bwanj…. Sindinganyoze joni ndinali yani ndikukhala ku nyasalandi koma mulungu anandichitila chifundo mpaka ndili joni moti pano ndinaphudzitsa geri aziphwanga ndi sisters ngakhale ger sinapitilize koma pano 2019 ndikukapitiliza ger nde winawe yomwe ukuiziwa spoon feeding kwamakolo ako nde plz uziyakhula bwino uwu ndimoyo…

  33. Sionse amene alibe kathu some of them they build good house they have properties that u don’t have they have money in their homes, don’t write your news like ur from Mozambique stupid

  34. Muwawonanso akubwelera komweko week ikuzayi anthu aketu ndi awulesi ndikulima anazolowela ganyu yoyitanila kawunjika Ku john ko.

  35. Inu pangani zanu! Mwatani kodi? unava kuti ali ku joeniko amangokhala osasungako ndalama ku Bank? Sibwino kutha malovu pa zomwe zachitikila wina pamawa ndiwe
    komaso mwayi wa munthu uli pena pali ponse kaya ndi mtown kaya ndi kunkhalango kapena ku joeni
    ndiye kumaupeza mtima please

  36. Deportee bambo sakutengera katundu kumalemba ngati munapitapo Ku xool ngakhale munaphuzira ya multiple choice. Amenewo mukuwaona ngati alibe poyambila koma pakutha masiku ochepa akuimbilani atabwerera mtima wa chikolopa bwanji Iwe uli ndi chani munthu oti umalandila R780. Mwezi onse Ku golosale uli ndi book la ngongole umakalembetsa mpaka kope kutha ndikusithitsanso

    1. Mukunamatu anthu ozolowera mavuto inu.Fans imene ikunziwa Jonzi boooo boooo singakhale Mpanje chifukwa cha deporteee abwelera pompano uwaonanso.

    1. Legister simcard koma malawi wandionjeza kungot pot adati zizindikilo zamasiku omaliza zzachitika zosiyasinasiyana nde adat zizachitika kumalawi konkha? Eish

    1. Ngati muli olemera pewani kuyankhula mozimva,mungayambe kutenga matembelero a Mulungu masiku ochepa ndikukhala mphawi kuposa ife.Ife amene timabwera ku Joni si anthu aulesi komanso tinaphunzira bwinobwino. Koma aliyense amene mutu wake ukugwira ntchito amadziwa mmene ku Malawi kukuvutira.Infact si anthu aku Malawi okha amene ali ku South Africa kufunafuna mwayi,kuli anthu kuno ochokera almost dziko lirilonse mu Africa,Asia,ndi mbali zonse.Ngati Mulungu wakudalitsani musamazimve kuchenjera.

    2. ndakumvan, but atleast suggest y they r being dhased if they r @ the rightful place. stop commenting just becoz ur uncle z among the victims but attach logical reasoning, I HAVE SUGGESTED LAZINESS & I CANT WITHDRAW THAT, wamva mwana wa mmbwenu nd mdyomba?

    3. Ukalemera udzilankhulira kuchipinda
      komaso ndibwino kuopa munthu osauka chifukwa sukudziwa kuchuluka kwa zinthu zomwe chauta adzamudalitse nazo mtsogolo

    4. #Wattie sakunama nonse mumathawira Jonz ndinu alesi, mbuli zachabechabe mumathawa kumudzi kuno kunatani, enafe sitigwira ntchito tikupanga survive bwanji? Azikuthamangisani choncho ndiye poti simumva mubwereranso

    5. Yes they nid 2 be smoked out they belong here ku Malawi enawo anathawa atapeleka zimimba kumamidzi kwawo alesi, manyaka awanthu

    6. ATonie tayankhulani mogwiritsa ntchito ma phunziro ndi mzerutu zomwe mulungu anakudalitsani nozozo,

      Inu tu ndi bigy ophunzira koma dziwanikuti anthu ena amapitaku Joni Ku ambiri ndikokasaka poyambira kuti azichita Tina busnes tao kumuziko mmadziwa kwathuko maganyu kusowa

      Tilindixifukwa zambiri zomwe sitinakhalile ma professor ngati inu NDA amzanuo
      Zoti mwina muthanso kutinvetsa

      Enafe mukanatipasa maganyu kulima mmunda mwanu kuti tipeze mpamba sibwezi tilikunoko

      Koma polimbikirapo palibe kumuziko,ulimi ukufuna fetereza mjomba

      So try to feel kuti mutakhala simunadalitsike munganve bwanji

      Tilipo ambiri mayiko osiyanasiyana ndipo timalimbikira ntchito zopweteka

      Kugwidwa koteloku ndivuto ndithu bwana

    7. Awattie
      Like my page Sparks Electrical and see what we are doing here

      We came her deported and rise up again pano tili ndi mapepala running our business and studying as well, very soon we will be oparating there !life is all taking risk
      Muziyankhulabwino

    8. Udakadziwa mmene anzako akutolela chikwama kuthebako sibwezi apa ukutokota zawusilu zakozi nyapapi wamunthu iwe
      Osangoyamika bwanji kuti naa ngati malawi akuwoneka bwino ndi anthu ovepha kuthebako mesa kugwidwako ndinthawi yawo nawo

    9. kwa amene akuti amene akupita ku joz ndi alesi mukunama chifukwa fanz ili kumeneko ndiimene Ikupangisa malawi kuti asinthe enanu pali inupo passport simukuiziwa ntengo wake guyz mukamalankhula muzizuyang’ana

    10. leave them Mr Joe mtima wa nsanje umenewo anthu akudya ma KFC kamba ka joni president Dr h kamuzu banda anayambira ku kugwira ntchito iye ndindani uyu sanavareso ndi tayi yemwe wochemerera ma min bus awa

Comments are closed.