Bingu Stadium robbers arrested

Advertisement
Bingu National Stadium

The suspects that took advantage of the current blackout to steal 15 Galvanized pipes which support a fence wire at Bingu National Stadium have been apprehended.

Following the incident, a manhunt was launched by the Malawi Police leading to the arrest of three people and confiscation of tools that were used to cut the fence.

Bingu National Stadium
Three people arrested over robbery at BNS.

According to Lilongwe Police, the theft occurred during the night of 20th to 21st December, 2017 at the facility when the law enforcers were patrolling the area.

This was the second time for the facility to be ransacked despite being just over a year old.

In April last year, thieves stole eight water taps at the facility that were installed in one of the toilets of the stadium.

Currently, the value of the galvanized pipes is not yet known.

The facility has no electricity due to unpaid bills of K25 million.

Advertisement

101 Comments

  1. ENAFE SITINALOWEMO NDIE AKUBASO AAAAA
    Ameneo don’t sentence them
    Bring them one day kukaZakhala game mzalengeze kuti akuba aja ndi awa!!!!!

    Tizalange tokha

  2. Stadium need to given to army or police and the perimeter be guarded by them

  3. Kuno ku RSA ndi dziko lolemera, ndiye mukufuna kundiuza kuti kulibe akuba? Kodi anthu enanu mmalankhula bwanji? Dziko la ameleka kulibe akuba? Ndiye inu kumalankhula kuti aa dziko la Malawi ndi umphawi ukuchititsa kuti anthu aziba, ndi zoona zimenezi? Ok, mukufuna kundiuza kuti boma lisiye kupanga chitukuko chifukwa choti dziko la Malawi ndi losauka? Nthawi zina, usanachite any comment, uzisiganizira kaye usanachete comment yakoyo.

  4. MOTI MPILA UKUKOMELAMU KU MW WINA MKUMAPANGA ZA MTOPOLA NGATI ZIMENEZI.AKADZATULU
    KA KUMENEKO,BURN THEM FROM WATCHING FOOTBALL FROM ANY STADIUM IN MW.

  5. KKKKKKK palibe chachitikapo apa umphawi wachuluka and umbana umachulukanxo chitha ndikubedwa chimenecho akusatira misokho yao kkkkk kenaka ku state house koko

    1. MUKUYANKHULA NGAT MBUZI ZA ANTHU. akumangilani stadium lero mukuti boma siliganizila achinyamata. oky.kuwabweleka ndalama amenewa angapeleke? muzionako zabwino

    2. Kkkkkkkk ine mbuzi yatonde kkkkk ndingongole baba from Chinese government moti tikubweza… Kmanxo BOMA ndi abbreviation so, try to find it’s meaning

  6. Mphoto yauchimo ndi imfa. Ankhaulitseni basi. Awapulumutse dyabulosi waoyo.

  7. Thats very bad and am sorry for hI’m coz kumalawi kuno milandu ngati iyi imakhala ndichigamulo chachikulu bola akanaba ma million a boma mkukhalaso wa ndale .

  8. Make an example of them!!! Selfish bastards…we can’t be vandalizing the little infrastructure we have !!!…lock them up and throw away the keys….kodi a Malawi tinakhala bwanji?

  9. Aaaaaaaa amalawi sazatheka basi,how they can steal water pipes and taps for what?just kubadwa ndi evil altitude

  10. good job for police but the good thing to do is just to kill them because they are people who don’t think and care about Malawi so why should we keep them burn them

    1. nanga dpp officials adaba ndalama enuakewo amkati blue night party. Chaponda adaba ndalama zogulira chimanga osewe sizidziwika kt ziripati. Lero busy kulimbana ndi wakuba mapipe kustedium, awasiye asangalale 2018 wabwino.

  11. dont leave them but punish them with a hard labour so that others can learn a lesson from them. munthu wamtundu wanji wodana ndi chitukuko.

Comments are closed.