We will come after you – Chilima warns

Advertisement
Soche hills

Malawi Vice President Saulos Chilima has warned people who have settled on Soche Hill that they will be evacuated even if they do not like it.

“This is a man-made death trap. People that have encroached Soche Mountain must be relocated and we will move them with immediate effect. I am serious on this,” said Chilima.

Soche hills
Encroachers on Soche Hill are refusing to leave

He also trashed the injunction the people who have settled on the hill have taken against their relocation.

“Nobody goes to court to get injunction against the dead following a natural disaster. Government will act,” he stated.

On his part, Blantyre City Council Deputy Director for Town Planning, Matthews Mwadzaangati, said the council was working on having the injunction vacated, adding that a site has been identified in Machinjiri for the relocation of the encroachers.

Advertisement

20 Comments

  1. Ine monga mzika yopanda mbali, ndili pa mbuyo pa ganizo la boma. Enanu kungoti simumawona za mayiko ena, mukazawona ku dziko la china, chilengedwe amachinyadira. Koma a Malawi ndi anyani, nkhwere za chabechabe ndi chifukwa zikumanga mu Phiri. I salute the VP.

  2. Mwawaona lero? Mose muja munali Ku Airtel simumawaona? Inu ma tower anu a Airtel mumamanga munsinje? Mesa mumakamanga pa phiri? Asiyeni nawonso amangaso paphiri akufuna network

    1. akakhudzidwa ndi mgozi Dpp yomweyonso idzikawononga chuma kumawasamala?? Dziko ndilathu ili a Malawi…how can one claim kuti m’ phiri muli malo ache?? kkkkkkkk….

    2. Apa palibe ndale anthu Amenewa achoke basi kumaona malo okhala.
      Boma lomwero ndilomwe lidzidzavutika ndi ngozi za dzidzidzi and Akati asadzachitepo kanthu muzidzati Boma silikusamala anthu awo….. Am not a DPP supporter but a concerned Citizen of Malawi.

  3. Ooo don’t tame a snake. Mwaziona tsapano,? Ndiye anthuwo akakhala kuti nanga muwapanga compensate ? Bwinotu paja kumachoka ma vote uku. U can say the truth but be carefull with pipple around u. Akupezerani chifukwa anzanuwa

  4. Koma inu zachamba zimenezo, Escom inapititsako kale magetsi, waterboard inapitsakonso madzi, kodi escom ndi water board ndi inu sikhethe kethe, tiziti samadziwa kut malo amenewo sololedwa? Asiyeni akhale basi zachamba, munthu mumamusiya amange kaye nyumba mkumamugumulitsa bwanjj?

Comments are closed.