Pavuta pa msika: Shuga wasowa

Advertisement

Zativutanso!

A Malawi ali pakalikiliki kuthamangila ku ma okala kuti apeze  nawo mwayi ogula shuga yemwe akusowa zedi mdziko muno.

Shuga wasala ochepa zedi mu magolosale aakulu ngati Shoprite, Peoples, Sana Cash and Carry komanso Chipiku.

sugar
Akusowa pa msika.

Malingana ndi  maripoti, izi zili chomwechi  chotele kamba koti kuli mpungwepungwe pa nkhani za mgwilizano wa pakati pa kompani yomwe imapanga shugayu ya Illovo komanso makampani onyamula shuga kuchokera kumafikitale kupitisa mmisika.  Koma a Illovo sanayankhulebe kalikonse pa za nkhaniyi.

Mu Shoprite mwachitsanzo munthu sakuloredwa kugula mapaketi opitilira asanu ndi limodzi (5) . Izi zaikidwa kuti aliyense aguleko shugayu yemwe akugulidwa ndi anthu mokanganiliana.

Izinso zapangisa kuti shuga afike pa mitengo ya K950 komanso K1000 kupyole mtengo ovomelezeka wa K750.

Mmene zililimu, pofika sabata la mmawa, shuga akhala atatheratu kamba koti mumagolosale ambiri watheratu.

Pakali pano bungwe lowona ufulu wa ogula la Consumers Association of Malawi (CAMA) lati kampani ya Illovo iyenera kunena ku mtundu wa a Malawi vuto leni leni la kusowa kwa shugayu.

IIllovo ndi kompani yokhayo yomwe imapanga shuga ku Malawi.

Advertisement

246 Comments

  1. Panja 2014 tikati ophuzila zakwanitsa wakhalapo kwa America ndiye rero ndizi maganiza kundetsa dziko ndichindu chobweka ngat kupalasa njinga tionana 2019 ngat zabereso galu amenowa ndalama zanthu zamisonkho mungodya muliphe inuwake ndikuvutika

  2. kkkkkkkk mbc news after the minister josephy mwananveka visited ilovo company,”sugar wa brown akusowa chifukwa anthu ambiri akumukonda”

  3. Anthu enanu muli m’mabvuto akulu ganyu wabvuta. Kodi panyumba kapena ndinene kuti pabanja zinthu zogwilitsa ntchito monga mchere,sopo,macheso,suga ndi zina zikatha amauza mwana kuti akapeze zinthuzo?Mwina kwinako zimatero,koma kwathu kuno timauza amene ali oyang’anira pabanjapo kuti athe kutithandiza.Ndiye ena mukuti tisaloze chala boma kapena pulezidenti ndiye chabwino tasintha inuyo inu tipatseni kapena tulutsani suga anthu asabvutike nkulimbirana pogula.Paja zinthu zikavuta olamula amakhalanso otsutsa muja idachitira UDF atachoka Bingu nkuyamba chake chipani ndiponso DPP idalinso yotsutsa nthawi ijayi atakhala pa mpando mayi Joice Banda pomwe dppyo ndiye inkalamula boma.Zinthu zabvuta kumpanda madzi achita katondo.

  4. Ndiwo Ana A Munthalika Ulamuliro Tidauzolowera Sizachilendo(chimanga Chochuluka,ndalama Kusowa,malipiro Kuchedwa,ngongole Zambiri Ndi Kusowa Kwamafuta Omwe Asowaso Posachedwa)komabe Timakunyadirani Poti Ntidziwitsa Kuti Sukulu Sichotsa Uchitsiru Moti Ulemu Wanu

  5. Many people r politicizing the issue of sugar scarcity.People who r pointing fingers at the president and his gvt r doing so coz of their negative attitudes towards the president.I know that people who r politicizing this issue r MCP and PP supporters.One word to u is that no matter how u spoil the image of the president,u shall not win the elections.Munyenyedwa kwambiri ndipo muzanamanso kuti mwaberedwa chisankho.Game simuzaiwona.For ur own information,shugayo wayambano kupezeka.Pezani nkhani ina yokamba

  6. kaya timwelalimozi juwisi inendamuzolowela mukut sugar mukanat mages ife tikanadandaula chifukwa mitembo ikananunkha mzipatalam

  7. Kodi sugar amene timagwiritsa ntchitokumalawi Amachoka kuti Moti akulowetsaso ndare ndishuga yemwe Koma Malawi uzasinthaliti Zilizonse Ndale Eiiish

  8. kodi anthu mumasiya kukupita nkhani mumaikhotetsa chifukwa chiyani?Peter amagwira ku ILLovo? mwangodana naye akukulamulanibetu musova.Ngati anabera simunapite naye kukhoti bwa?munali kuti?wabwino mudzampeza kuti? Mudzandifunse,Mcp yopha anthu,Udf yodula mabere kuChiradzulu Pp yodula ziwalo.Ali mwana ndindani yemwe samaona ?Ndinu womvetsa chisoni etiii? shamefull

    1. vuto si iwe koma mutu nzeru zero,umafuna amalawi aririre nda ,kodi tikamati mtsogoreri akutandauza cha? athu ena chithupi kungokula nzeru kumanja,stupid !! u must shut yo fucken mouth

    2. Unaiwalaso dpp yopha albino.Boma lilindimphavu pamalonda ndi chifukwa kuli nduna yazamalonda sikuti imangoyang’ana makapani aboma okha ngakhale Illovo ndie akuyenera kulowelererapo.Iwe ukuganiza kuti a Malawi tonse tingapite ku Illovo kukadandaula??????????

    3. Kodi A Malawi Mudzapenya Liti? Kodi Simudziwa Kuti President Ntchito Ina Ndikupanga Overlook Ma Company Akuti Akugwira Bwanji Ntchito, Mwaiwala Atasowanso Sugar Mu 2012 Zinatengera Joyce Banda Kulamula Kuti Sugar Apezekenso Nde Muli Peter Amagwira Ku Ilovo? Ngati Ma Kampani Sakugwira Bwino Ntchito Dziko Lingatukuke Bwanji ? President Akuyenera Kuchitapo Kanthu

    4. komatu tinawaona olemekezeka a mwanamveka akuyendera sugar factory pa tv ndipo anapanga confirm kuti sugar ayamba kupezeka. nde iwe kadet ukuti boma sizikulikhuza bwana mwanamveka amakataniko ku ilovo ?

  9. No wonder, that’s DPP Govt…

    A Malawi tinazipalasila tokha makala amoto pa zisankho za mu 2014…

    Nde tiliradi ndipo sitinati

    vuto losankha anthu oipa, opondereza, adyera komanso ankhanza kuti atisogolere ndi limeneli…

    Next is fuel…

  10. Eeeee akuti Amalawi tavuta kwambili Illovo yaganiza zoyamba kupanga pack mphendo zamzimbe Muma packets tizingofinya tokha…. so bad

  11. Paja sugar factory ili ku sanjika ndi ku new state house etii…. by the way magetsitu atsiya kuthimatu… world bank has resume….kkkkk izinso Lembani mosindikiza ndithu

    1. I need to be schooled if at the moment we have alternative to that….. standing on our own it’s gradual thing not kungozuka lero

  12. kumalawi mumamwa tea ndinu opezako ndalama. ife tilibe nazo ntchito zimenezo olo atasowa kwa zaka ten. timadya nsima mamawa komanso pena kukazinga chimanga.

  13. Chinthu Chikalakwika Koma Kunyoza Kokha Kokha.World bank yapanga suport budget mwakwiya sugar wasowa pamsika mwakondwa kwambiri amalawi mwatani? peter mukumunyoza mwina 2019 azalowanso m,boma.

  14. Stupid!!Onama Inu Lero Lomwe Ndinali Kogura Ndakumana Ndi More Than 10 Pple Atagura Ma Bale A sugar Each In Limbe So What Do U Want To Say Idiots

  15. A Illovo amapanga zotiyesa,akufuna anene kuti mzimbe zinauma? panopa madzi ndi ambili sugar akumasowa nanga october ndiye bwanji? koma malawi bola nyasaland ija.

  16. za ziiiiii kod kusowa kwa shuga ikhale nyimbo???? not all of us can afford to have tea gyz,,,,,,kaya kwa mene amamwa tea wo zao zimenezo

  17. One to blame is not Government but Illovo. Illovo started before Peter Mutharika even before Bakili Muluzi. Why you blame innocent person. Think before you comment

    1. The government is industry regularator and over seer and is also to blame.Why the government hold ministerial of industries? They are at the helm!

    2. To Limbe Addison. Am not here to fight with anyone. What you should know is that Facebook is for charting not swearing each other. If I talk something wrong to you Just forgive me and you are the first person to talk like that. We just put a comment about our Government not friends. So mind your tongue.

    3. koma tu zinazi let’s take our feelings aside n think ….I don’t think its the duty of a president kuwona kuti sugar alipo nyumba mwanu or Ku shop rite …illovo is not a govt department… The main problem with us is this monopoly capital companies like carsberg mW..illovo etc …if we had other companies in the sugar industry we couldn’t b this worry… Right now what’s needed is for illovo to explain to its customers not pres must explain to illovo customers no no ….

    4. Ena nkhani ya sugar ailowesa ndale.This shortage of sugar has nothing to do with Peter Mutharika.Ena mukhoza kumanena kuti he is a failure.Maybe u hv to find other reasons to name him a failure not this sugar issue.Mind u wayambano kupezeka pano shugayo.

    5. sugar wasowa tili mu ulamulilo wa ndani wa “peter” tiyenera maso anthu kuyang’ana kwa iyeyo, nanga ma company ena mukuwanenawo angawayitane ndindani oposa goverment nanga government yo akuyenda ndindani president, nde zosezi ndi gwero lake watch ur taque dis guy is a failure dat’s all palibeso chifukwa chumuyikila kumbuyo ameneyi eish !!!

    6. Kodi Pali President yemwe anakwanirisapo zofuna as wanthu? The answer is no. Ziko latthu langokkhala losauka basi. Ngakhale patabwera mogoleri wina tizalirabe mpaka kale. Chofunika ndikumangopemphera kuti tizipeza chakudya cha lero osati tea ayi.

  18. Kwathuku ngakhale atazalamulilandani sikuzathekanso kubwelela chikale ndipo amene akumakakamila kuzalamula apa akungofuna njilayoti anthu azizawatukwana Ooo Allah chonde chonde chonende lipangeni zikolathu la Malawi kuti lisazafike pamavuto ngatimmene inalili Zimbabwe muma 2003 eshiii izindiye zinanso zozilimilatu zimenezo

  19. We are yet to hear from Illovo what is the problem!!?
    Pangatalike bwanji we shall hear the cause for this becoz others are saying illovo wanted to finish white Sugar which was remaining at their warehouse.

    1. Illovo has given its version of the story, when the trade minster paid them a visit some days ago.
      They have doubled their effort soon the market will be flooded, like here in Lilongwe both brown and white is everywhere now.

  20. Zayambiranso za mkuluwake zijatu kkkkkk kenako mafuta kkkkkk boma iloooo!!!! Zilibho mulungu wakwiya ndi anthu obera mavoti chilichonse chikuyang’ana kukhoma ngati Ahabu m’baibulo kkkkk

    1. Ngwazi the problem is that they underestimated the sugar thereby exporting more and some sold locally to major companies like Calsburg, chibuku, universal etc, the stucks for local consumers is empty. However this years production has started last week and it will hit the market soon. For us we have already started consuming

  21. hehehe koma zodandaula za anthu sungazimvetsetse,ife tikati tamwako madzi otetha ndiye kuti tapungula nsuzi wanyemba kapena nsaula.Breakfast yathu ndichimanga chokazinga mulunena za sugar thuni eiiish athu mulujoya atiiii???

  22. There z something behind musayiwaletu paja zinachitikanso 2012 atalowa mayi joyce banda sugar anapezeka ndipo anatsika mtengo ndipo a illovo ananena mu chikalata chomwe chinalembedwa kuti anachita dala chifukwa president wa nthawi imeneyo ankachita demand ndlama za pa dera zopitira kunyanja ndi dzina zotero so lets expect hard times again

    1. That’s very true, the commodity became scarce the time we were about to lose bingu. I was in mzuzu that year and it was 1 packet per buy(characterised with queues) in Peoples @K800/1kg packet from something like K350. We all know what followed later.

    1. Akulu boma litha kuyankhulapo ndilomwe limapeleka ma licence! Bwanji za magetsi mmaloza chala boma, limapanga magetsi! Nanga akati unduna wa ma factory, boma liti ndi ma factory mu cingerezi boma NRI over seer and industry regulator work up!

    2. Illovo is private company,if there is any problem is for Illovo not government,,Escom is a government company if theres a problem is for govrnment…This is for Illovo to sult out.

    3. Evance Charlie you need to be schooled, Government is a esponsublr to regulate issues of national importance, its like you don’t know, Government have 15% shares in Illovo,65% belongs to Malawians and 20% is for illovo .We have Ministry of Industries, should we say Ilovo can’t listen to the orders made by the minister? You need to go back to school and learn much how things work.

    4. Evance Charlie wandimvesa chisoni bwanji! Anthu enanu zinthu zikamakhala chontchi, zimakusangalasani eti? Kodi kumakhala kukonda chipani? Tamakhudzidwani ndi za mu dziko anthuni

    5. pali athu ena ngakhale ku family yakwawo ,akuluza nawo ,u must think wise ,amalawi apo ayenela kufusta astogoreri awo ,some important questions sugar uja timagula allikuti ,mbuzi zina pamenepo zikuti eti ,boma limapanga sugar ,iwe ndiwe garu yeni yeni

    6. Ameneyu osakutaya and amvere radio ngati Ali nayo, Boma latulutsa press statement pa za sugar, nanga apanga izi kaamba ka chiyani? Umbuli a Evance changamukani!

  23. kaya kwamene amati akapanda kumwa tea amakhala ngat aotcha mzikitiwo ife unatilimbatu.sunday ndmacheza ndi brother wanga frm Dwangwa tnakumana ndimoz mwa omwe amapanga nawo sugar ku Dwangwako,ndikumufusa kut kod akulu takambani y sugar akusowa chonchi????? ali mbale sugar tinapangatu okwanilatu mpaka amasowa pokhala komano vuto,kunabwera Vice president waku Tanzania ndpo anagula sugar oculuka zedi mot anacita kulesesa amafuna asese yense.nde kupezeka kut wina yemwe analipanja amasowa maloyo ananyowa ndi mvula mot alibiiii sangathe kupitisa pa nsika,koma nkhani yaikulu ndiyakut sugar anagulisidwa ku Tanzania.SHAME!!!!!!

  24. Kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkmmmmmmm ife ndi a nsima

  25. ayi zachita bwino amphunzirepo chimphunzinso a #ILOVO zoti anthunso akunja amagwiritsa yemweyo sakuziwa? nthawi zonse mumangopanga zinthu zoyerekeza~mumayetsa makoponi? tiye nazoni munva kuwawa …..!!!

    1. musazanamizidwe kuti kunja amagwiritsa illovo.that is a big lie.kunja kwake kuti.? munthu ukakhala kuti sunatendepo umangonamizidwa chilichonse ndithu.

    2. a #damien zoti mumagwiritsa ntchito grade 3 simumaziwa? inu mumagwiritsa ntchito ma residures grade 1 and 2 simungamununkhe inu a #malawi… go and make some enquiries den u come back with a tangible report not diz….!!!

    3. inu a #damien zoti sugar mukugwiritsa ntchito kumalawi ndi grade 3 mumaziwa? ok nde ufufuze kuti grade 1 and 2 amapita kuti simungamununkhe a #malawi or pang’ono ataa!! ngati ukufuna ma umboni a izi ndikuyankhulazi utume atola nkhani ndizayankha….!!!

  26. Our sugar is produced locally and with a local supply of raw materials. How come now this scarcity. I can see that the current government doesn’t care for its citizens at all. They are failing their mandate to provide essential services to the people.

    1. my men govt diesnt not peoduce sugar, but illovo.here at illovo there was a machine breakdown for three month now.oti machine ayamba kuyenda dzana.uasamangoblamer boma Zilizonse.

    2. Bwana Damien Jhala..I did not say that the government produces sugar. Re-read my comment and understand it better. It is the government’s responsibility to ensure the availability of all basic human needs to every citizen of the country one of which is food in which sugar falls under. It not only Illovo that produces sugar in Malawi as far as I know. Did the machines also break down in the other sugar producing companies? It is again government’s responsibility through the Department of Trade and Industry to convince foreign investors to come and invest more such industries in the country if the current ones cannot meet the quantity and requirements.

Comments are closed.