Man breaks into Malawi State House

Advertisement
kamuzu-palace-

A mad man managed to make his way into the Kamuzu Palace in Lilongwe even though the house has several checkpoints, Malawi24 can report.

kamuzu-palace-According to reports, the mentally ill man was found sleeping in a waiting room within the palace before officers on duty managed to detain him.

The man has since been taken to Kawale police for questioning but is expected to be sent to Zomba mental hospital soon.

The incident follows another one involving a large python that was found at the Kamuzu Palace over some months ago.

During late Bingu wa Mutharika’s era, the palace was reported to have been stormed by ghosts.

Advertisement

197 Comments

  1. Anthu inu simukuziwa chilichonse ndi Ana inu peter ndi wakulu sangakhale alibe kenakake inu state house wamisala alibe mpata olowa iye ndi zomwe peter amasunga nyumba mmo ndiye watha mphamvu zake zomwe amasungila bola kuthaya akhale ngati wamisala ukafunsa monva kuti ndi mulomwe wa kuThyolo pa 6 miles

  2. zikolilommadzi chitetezo palibe ndikunyumba ya malamulo yomwe!!!!!!,eeesh!!!!!!!!,akanamupha peter n’kada wathu eee!!!

  3. Ngati munthu adakwanitsa kuwadutsa ma Swiss guarsds ku UK ndikukalowa ku bedrum kwa Queen ka state house ndikachaninso

  4. eeesh! how did he managed to to reach there since the house has several checkpoints?were the guard drunk?oooo!! maybe he booked an apointment with mr presdent acoding to new year kkkkk

  5. eeesh! how did he managed to to reach there since the house has several checkpoints?were the guard drunk?oooo!! maybe he booked an apointment with mr presdent acoding to new year kkkkk

  6. Very strange. Where were the security personnel? Please they need to be transferred from the State House. This is unusual

  7. That’s a great achievements to us mad people. I hope my fellow had a petition to express to the man there. Don’t blame the guards. May be he followe good and all strategies to see our good first citizen. In the bible remember the parable of the invitation to the banquet (feast) he might be also invited by professor to give farewell to 2016. congratulation the mad man!!.

  8. i have heard from Dairy Times News Paper Of 20 December 2016 page2 that the guards at state house have not been paid their allowances for 6months now,just imagen!!!! can they perform well? someone is fooling someone here,, lets not just blame guards here,blame the bigman himself&his peter mkhitho for not mobelising there guardmen.. zikuwoneka zophweka apapa but imagen akanakhala criminal? things are not ok here.

  9. Mwati mumalize chakachi ndibodza limeneli, social network zapa Malawi kuyamba chaka ndibodza ndikudzamalizaso ndibodza. Zaku Statehouse palibe amanena zoona, kumbukani zija mumkaika masamba Ku statehouse kuti APM wafa, abodza anthu oipa inu, naa zaku statehouse sindingakukhulupilileniso

  10. even a mad person thinks reasonable enough n knws who has failed malawians. While bootlickers aka cadets thnk all these blackouts n the stinkn ministry of agriculture z devlopment.

  11. Paja wamisala nthawi zina amatha kupanga zinthu zosokonekela like kugenda, kuswa zinthu, ndiye tiyelekeze apapa akanati waotcha moto kumeneko kapena wawagenda a president pamphumi ndikuwavulaza tikadamati ndi chani? this completely shows that even security is there but anything can still happen, which means God is the only solution interms of security, these bodyguards can fail us

  12. ameneyo siwamisala ayi wachoka kumudzi wakadzionetsa kwapresint kuti akuvutika mudzi misonkho yao sikuoneka chochita mdziko muno kuteroko amakasuma kwa pitala asamangodya okha kupalace kkkkkkk azikhala komweko ikhala nduna yachitetezo basi

  13. kkkkkkkk koma Zoona Zimenezi?Ku state Ungapite Mwa Chisawawa Ma Camera Oseaja Ndekuti Samagwila Ntchito Kuti Amuone Opengayo?kkkk Komatu Inu A 24 Muzinena chilungamo.

  14. ndipomwe mwadziwira kut mulungu simunthu komaso simwana, mulungu sanakhalepo wamisala kapena robot lomaseweredwa tsiku ndi tsiku, ukulu wake waonetsera kut utsogoleri ulipowu mulungu sanakondwere nawo komaso sakukondwa nawo paka kale kale,sangalore kut dairy aziwona ana ake akuzuzika ndi kulira chifukwa cha munthu imodz yomwe akusokoneza ndi ku zunza mizimu ya anthu osalakwa , uku akumuonetsa kuti mulungu ndiwakulu atembenuke mtima ndi kumvera zofuna mulungu

  15. Security guards were all drunk at the time this guy breakthrough…lets be honestly this mad was tired of searching food from the empty bins bcz there is no food in the country

    1. You are right #pempho, and this is the also a straight forward sign of security lapse in malawi and therefore security personnels at the state house must face chop with immediate effect. “otherwise if the man is mad indeed, why quetioning a mad person”??? those who are questioning him i believe they are also mad more than him!!!!

  16. izozo nde zofuni zoona president wathu kumachita kupanga booking kt tikamuone asali pa udindo umenewo timangopita ife kuden kwake no vuto

  17. Kuipa kolembera tchito ndale komaso ubale ndikumeneko! They are not professional presdential guards. Ngat wauwisi ukuyaka chonchi nanga ouma utani? Miyoyo yathu ili pa chiwopsezo ndithu

    1. its indeed a shame, i also heard from Dairy Times News Paper of 20 December 2016 that these guards have not been paid for 5months now, can they perform??? something is wrong somewhere..

  18. Michael Mkunga Khilistina M Dombo Dombo Bornface Chitengu Lawrence Botcho Ronex Shadreck Biason Botcho Allan Mtukula Alefa Amon Banda Thomas Naison Phaless Makupulah Florence Banda Tedius Khokhokho Aloni Zakaliya Stanford Khipala Fainess L Chauwa Fales Weniweni WA Doreen Joyce Mofokeng Bishop Harry John Franciscal Dar Joel Rose George Diliro Wa Ander-son

  19. Inu vimalonda mumatani,mbuzi inu,mukufuna presdent wathu afe?inu busy kumalimbana ndi mighty chakwera,mkusiya zitseko zosatseka,ndakwiya nanu.

  20. Anthu anakwanitsa kugumula pentagon malo omwe ndiiotetezedwa kwambiri padziko lonse lapansi.
    Ndiye chachilendo ndichani ndi state house

Comments are closed.