We are not aiding abductions – Police

Advertisement
Albino

Police in the Eastern Region have denied reports that they are playing a role in the killing and abduction of people with albinism.

Reacting to accusations which were made by traditional leaders in Machinga, the region’s community policing coordinator, senior superintendent Alfred Chimwaza said the police are not helping the criminals.

Albino
Albino attacks on the rise in Malawi. (Google images)

“I think the problem is that everyone thinks different from another, I suggest that there can be other officers with such ideas. People should know that we are not aiding albino’s abduction but we are against it,” said Chimwaza.

He added that the law enforcers are working tirelessly to make sure that people with albinism are enjoying their rights just like everyone.

Cases of people born with albinism being abducted and killed have increased in the eastern region especially in Machinga and other surrounding areas and this has prompted Eastern Region Police to conduct interface meetings with villagers in the district.

 

Advertisement

44 Comments

  1. Apa tisacedwepo apitala angolamula kuti 2weeks yokha anthu opezeka akuenda nite azibenedwa popanda mulandu muona izitu zicepa plz cifukwa azolowela.

  2. ife kuno ku nsanje tikawagwira anthu Okupha azowo ife timangowaotcha basi ifa kwa ifa Moti pano Utsilu Ophanawo wachepako kuno

  3. Chofunika muwalembe ntchito ya police ma alubhinoyo then ena muwalembe kukhotiko tione ngati mchitidwe opha ma lubhino ungapitilire akachama pangani zimenexo bac muona result yake

  4. Chofunika muwalembe ntchito ya police ma alubhinoyo then ena muwalembe kukhotiko tione ngati mchitidwe opha ma lubhino ungapitilire akachama pangani zimenexo bac muona result yake

  5. Nkhani zinazi sizoyeneranso kulimbana ndipolisi….deal ndiyokuti anthu oterewa akagwidwa akuyenera kuphedwa nawo same time. mwina nchitidwe onyansawu ungathe

  6. Amene atapezeke ndi mafupa awotcheke or aphedwe. Apolice yawo ndi bzns bas. Asatipase ma bzy ndi kudandawula pamene abale athu akutha.

  7. Asakane amenewo. Ali mbali imodzi ya zigawenga. Bwanji akumawamasula anthu okuphawo? Milandu yokupha imakhala ndi bail? Ngati Mulungu sakulangani pa dziko lapansi lomweli, adzakakulangirani ku Gehena

    1. Malamulo aziko lino amapeleka ufulu kwa munthu wina aliyense kupasidwa bail ndi court pa mlandu uli onse. Kunena zoona anthu oganiziridwa kuti anapha munthu koma sangathe kupeza lawyer ndi omwe akuzuzika ku limandi koma olemerawa a alibe problem, so we have to criticise our weak constitution (laws) which provide rights to murder suspects to be released on bail.

  8. Ngat mdzika yadziko lino ndiudindo wanthu ifenso kuteteza maufulu azanthuwa nt only the police chifukwa wapolice ndimunthu ngat ife tomwe. Kmanso anthu amene akuphedwawa ndiabale anthu ndiye tiyenera kutengapo mbali.

  9. Godfry I no kuti police simapereka chigamulo koma Judicial brach ndemundiwuza kuti tiblame judicial brach? Pakuti chitetezo chose chilimmanja mwa apolice.okoni panopa Godfry kuti wapalamula nde police yakutenga pakagalimoto kawokaja mkukakutsekela ngati uli ndi makwacha mawa ubwelako pamenepa khoti lilipo? Police too much crapition pa nkhani ngati izi man Godfry

  10. Godfry I no kuti police simapereka chigamulo koma Judicial brach ndemundiwuza kuti tiblame judicial brach? Pakuti chitetezo chose chilimmanja mwa apolice.okoni panopa Godfry kuti wapalamula nde police yakutenga pakagalimoto kawokaja mkukakutsekela ngati uli ndi makwacha mawa ubwelako pamenepa khoti lilipo? Police too much crapition pa nkhani ngati izi man Godfry

  11. Blame game will not assist in ending the issue at hand. Security is a corrective effort, don’t let it for the Police only. For your information Police work is simple when members of the community provide tips and information to them,,,,, people know the perpetrators of crimes and hide the information to Police, how do you think crime will be reduced or stamped down? and for your information Police duties is only to investigate, arrest, prosecute or take the case to court and judgement lest in the hands of the judges in tandem with what the laws say.

  12. Blame game will not assist in ending the issue at hand. Security is a corrective effort, don’t let it for the Police only. For your information Police work is simple when members of the community provide tips and information to them,,,,, people know the perpetrators of crimes and hide the information to Police, how do you think crime will be reduced or stamped down? and for your information Police duties is only to investigate, arrest, prosecute or take the case to court and judgement lest in the hands of the judges in tandem with what the laws say.

  13. Kodi ngati mumapha alubino analakwa chani please mulungu sangalenge chithu chopanda phindu mwina ndichifukwaso ziko lamalawi likukumana ndi zowawa chifukwa mukupha athu osalakwa

  14. Kodi ngati mumapha alubino analakwa chani please mulungu sangalenge chithu chopanda phindu mwina ndichifukwaso ziko lamalawi likukumana ndi zowawa chifukwa mukupha athu osalakwa

  15. Michael>point of collection,the Malawi Police is not the 1 who passes judgement on somebody’s case(s) thus they not really the 1 to blame.Ofcours they r categorized in the judicial brach of the regime but judging is not there course

  16. Nde tiblame ndani? Poti anthuwo mukagwira mukumawatulutsaso apo zii kuwapatsa zaka zochepa 5year prisoner mulandu wakupha nayeso akakhale moyo wake wose kundende koma 4 year anthuwa chilango chikuwachepela.nde apa mukuti tisa blam police why? Eee inu mukudyanawo chamagazichika akumakupatsanikoni makwachawa

  17. Nde tiblame ndani? Poti anthuwo mukagwira mukumawatulutsaso apo zii kuwapatsa zaka zochepa 5year prisoner mulandu wakupha nayeso akakhale moyo wake wose kundende koma 4 year anthuwa chilango chikuwachepela.nde apa mukuti tisa blam police why? Eee inu mukudyanawo chamagazichika akumakupatsanikoni makwachawa

  18. They need to dny that bcoz akagwila the suspected people amalandila ziphuphu mkuwamasu without being judged ndie akutengapo gawo

  19. They need to dny that bcoz akagwila the suspected people amalandila ziphuphu mkuwamasu without being judged ndie akutengapo gawo

Comments are closed.