Flames climb on FIFA rankings

Advertisement
Flames- Malawi
Flames- Malawi
Flames-; Up on world ranks.

The Malawi national football team have climbed up by two places to 104 in the World and 28 in Africa in the latest official FIFA rankings for February 2016.

The Enerst Mtawali’s charges have slowly moved up the latest FIFA rankings ladder despite not playing matches since the Cecafa tournament last November.

The team was out of action since losing 2-0 to Uganda in the quarter-finals of the Cecafa cup.

The Flames are also not part of the teams at Chan tournament in Rwanda. Malawi will face Equatorial Guinea next month in a crucial 2017 African Cup of Nations qualifiers away from home before hosting their opponents four days later.

Belgium remains World’s best seconded by Argentina with Spain and Germany coming third and fourth respectively.

Ivory Coast are the highest ranked African team in 28 position, with Cape Verde Islands, Algeria and Ghana the next highest in 33rd, 36th and 41st place respectively.

Advertisement

151 Comments

  1. Mubwere ku Mangochi inu ma players Tizizalima fodya mwamva.

  2. I Think Izizi Zilibe Ntchito Koma Yambani Kukonzekera Mipira Imene Ikubwera Kutsogoloku

  3. bola nthawi ya kina ma cuash enawa amangowononga mbili ok anway

  4. Kodi dza ma Fifa ranking izidzachabechabe malawi yapanga chiyani choti ikakwele ? No friendly matches nde wina mkumasekelela zimenezi .Ndidzaombela mmanja ngati flames itapezeka ku Afcon 2017 apo biii za ma Ranking zilibe film kwa ine

  5. Kodi dza ma Fifa ranking izidzachabechabe malawi yapanga chiyani choti ikakwele ? No friendly matches nde wina mkumasekelela zimenezi .Ndidzaombela mmanja ngati flames itapezeka ku Afcon 2017 apo biii za ma Ranking zilibe film kwa ine

  6. Thanks to national team your makes us to known by the world no matter we are disappointed most times we still have our trust to frames muwauzekoso akutiberawo kuti akamasolola azitiganizirako oukondafe

  7. Thanks to national team your makes us to known by the world no matter we are disappointed most times we still have our trust to frames muwauzekoso akutiberawo kuti akamasolola azitiganizirako oukondafe

  8. Koma amalawi tili ndi vuto m’malo molimbikisa team yathu ndipamene tikunyaza sitikonda dziko lanthu ndichifukwa sitimachita bwino,for instance ajibuti munamva akunyoza team yao ikaluza.koma ife vuto ndi chani?

  9. Koma amalawi tili ndi vuto m’malo molimbikisa team yathu ndipamene tikunyaza sitikonda dziko lanthu ndichifukwa sitimachita bwino,for instance ajibuti munamva akunyoza team yao ikaluza.koma ife vuto ndi chani?

  10. There is nothing to smile about,the next thing the same flames will disappoint the whole 15million Malawians home Or away .A Malawi sitichedwa kuiwala????.

    1. Lol!!!! Sitichedwadi kuyiwala.Their body language shows lack of effort.Look at their faces they smiles when they failed,no regret or anger!!!!!!!!!!!!!!!!!

  11. Mmmm palibe chanzeru apa bola nkupezeka mu top 10 koma nanga mpaka 104 ndiyenso nkumanyadira munakhalabwanj amalawi

  12. Mmmm palibe chanzeru apa bola nkupezeka mu top 10 koma nanga mpaka 104 ndiyenso nkumanyadira munakhalabwanj amalawi

  13. Azingosamala osagona coz our nxt gme against Guinea xixocheza Guinea is on fire don’t relax with dis Fifa rankings dey r notin widout qualifying to 2017 afcon 2010 lija nd kale anyway well done to dem

  14. Azingosamala osagona coz our nxt gme against Guinea xixocheza Guinea is on fire don’t relax with dis Fifa rankings dey r notin widout qualifying to 2017 afcon 2010 lija nd kale anyway well done to dem

  15. nanga apa pali chonyadira a Malawi 24?zaonetseratu kuti mulibe chopanga report ……tatiuzeni kuti a police amenyedwa aja pano akupeza bwanji kapena alipo wapitilira?

  16. nanga apa pali chonyadira a Malawi 24?zaonetseratu kuti mulibe chopanga report ……tatiuzeni kuti a police amenyedwa aja pano akupeza bwanji kapena alipo wapitilira?

  17. palibe chanzelu apa fight hard netx tym tizamve muli pa number 20 pa word and mu Africa number 2 zizakhala bwino koma izi ndizosakhala bwino to be honest

Comments are closed.